[male
vocals] 1
Ndikonda
Mlungu
pomva
Mbuye
wanga
Amva
pemphero
ndi
kulira
kwanga,
Namatchereza
khutu
nditapfuula,
Andithandiza,
nandipulumutsa. 2
Mulungu
wanga
ndiye
wachifundo
Ndiwolungama
mtima
ndi
wabwino;
Apulumutsa
anthu
akufoka,
Akathandiza
nkhawa
imachoka. 3
Mtimanga,
bwera
kuti
upumule,
Wakuchitiranso
zokoma
Mbuye,
Wakuchotsera
imfa
ndi
misozi,
Ndingakhumudwe
asungira
phazi. 4
Nditani
ine
kubwezera
Mbuye
Zokoma
zonse
anandichitira?
Chipulumutso
chake
ndidzatama,
Ndinalumbira
zija
ndidzapatsa. 5
Imfa
ya
anthu
ake
imkomera,
Awalandira
m'nyumba
zokonzeka,
Mbuye,
kapolo
wanu
ndipereka
Nsembeyi
yonga
yanu,
ndine
ndekha.