(Yaaaa
eye) (
Eee
Naadi
pano!) (
PS
ONE
MAN
MJDC-Goma)
Yeah,
yeah
Zimakhala
choncho
nthawi
zina
Ukaikonda
mtima
wako
pa
munthu
mmodzi
Zimapweteka,
m'mutu
umababa
Yeah,
mvetsera
Ine
ninkhala
mutu
umababa,
why?
Because
I
love
you
Ine
ninkhala
mutu
umababa,
why?
Because
I
love
you
Manje,
why
umanichokamo
Baby?
Umanichokamo
why?
Bebe
Nthawi
zonse
ndikafuna
kukhala
nawe
Iwe
umawoneka
ngati
ufuna
kundisiya
Mtima
wanga
ukupweteka
ngati
wathyoka
Ndikufuna
iwe,
sindikufuna
wina
Ine
ninkhala
mutu
umababa,
why?
Because
I
love
you
Ine
ninkhala
mutu
umababa,
why?
I
love
you
Manje,
why
umanichokamo?
Baby,
umanichokamo
why?
Bebe (
Yaaaa,
leka
nikuuze)
I
PS
ONE
MAN
MJDC-Goma
Ine
nimakunda
ngati
bingiza
namavi
E
e,
ine
nimakunda
monga
mata
nalulimi
Ya,
ya,
ine
nimakunda
monga
mbowowo
nakutu
Baby
nimakunda
monga
meso
namisozi
That's
why
am
saying,
why?
Kodi
ukufuna
ndipite
kuti?
Mtima
wanga
uli
pa
iwe
wekha
Sindingathe
kukuyiwala,
sindingathe
kusiya
Kukonda
uku
nkoopsya
koma
nkokoma
Ine
ninkhala
mutu
umababa,
why?
Because
I
love
you
Ine
ninkhala
mutu
umababa,
why?
I
love
you
Manje,
why
umanichokamo?
Baby,
umanichokamo
why?
Bebe
Si
kuseka,
si
kusewera
Ndikunena
zoona
zochokera
pansi
pamtima
Umanichokamo,
umandipweteka
Koma
ndikadali
wako
mpaka
kalekale
Palibe
wina
adzatenga
malowo
Ndiwe
wanga,
ndine
wako
Ine
ninkhala
mutu
umababa,
why?
Because
I
love
you
Ine
ninkhala
mutu
umababa,
why?
I
love
you
Manje,
why
umanichokamo?
Baby,
umanichokamo
why?
Bebe (
Yaaa
leka
nikuuze)
PS
ONE
MAN
MJDC-Goma
Mtima
umababa
chifukwa
chako
Usandichokemo
baby
Ndikukufuna
iwe
wekha (
Yeah,
yeah,
yeah) (
Eee
Naadi
pano!)