[male
vocals] (
Reggae
rhythm
kicks
in
with
a
steady
bassline)
Yesu,
yesu,
yesu.
Mundimvere,
Mbuye
wanga
Nkana
ine
ndimalakwa,
Koma
ndinu
moyo
wanga;
Mbuye,
mkhale
ndine.
Mbuye,
mkhale
ndine.
Mbuye,
mkhale
ndine
Mbuye,
mkhale
ndine
Ndine
mlendo
pansi
pano,
Msanditaye
m'dzanja
lanu,
Mundisunge
mwana
wanu;
Mbuye,
mkhale
ndine.
Mbuye,
mkhale
ndine.
Mbuye,
mkhale
ndine
Mbuye,
mkhale
ndine
Munafera
ine
kale
Kuti
mukandimasule,
Lero
lino
mndinyamule;
Mbuye,
mkhale
ndine.
Mbuye,
mkhale
ndine.
Mbuye,
mkhale
ndine
Mbuye,
mkhale
ndine
Mundidzze
ndi
chikondi,
Mndiyeretse
m'mtima
monse,
Chifuniro
change
mthyole;
Mbuye,
mkhale
ndine.
Mbuye,
mkhale
ndine.
Mbuye,
mkhale
ndine
Mbuye,
mkhale
ndine
Imfa
ikandifikira,
Inu
ndidzakangamira;
Ndikalowa
ine
m'mdima,
Mbuye,
mkhale
ndine.
Mbuye,
mkhale
ndine.
Mbuye,
mkhale
ndine
Mbuye,
mkhale
ndine
Yehova,
Mbusa
wangadi,
Ndilibe
kusowa;
Andigonetsa
bwinoli
Mumsipu
wokoma.
Cha
dzina
lakelo.
Ku
madzi
ake
odikha
Anditsogolera;
Ndi
moyo
wanga
wofoka
Aulimbikitsa.
Anditsogolera
m'njira
Zakulungamazo;
Chifukwa
changaay',
koma
Ku
madzi
ake
odikha
Anditsogolera;
Ndi
moyo
wanga
wofoka
Aulimbikitsa.
Ndipyola
kodi
chikhwawa
Cha
mthunzi
wa
imfa?
Ndilibe
mantha
ngati
'Nu
Mundiperekeza.
Ku
madzi
ake
odikha
Anditsogolera;
Ndi
moyo
wanga
wofoka
Aulimbikitsa.
Chakudya
changa
chabwino
Mwandikonzera
pha!
Pamaso
pa
adaniwo
Mudyetse
mtimanga.
Ku
madzi
ake
odikha
Anditsogolera;
Ndi
moyo
wanga
wofoka
Aulimbikitsa.
Mwadzoza
mutu
wanga
ndi
Mafuta
okoma,
Mwadzaza
chikho
changadi,
Inde,
chisefuka.
Ku
madzi
ake
odikha
Anditsogolera;
Ndi
moyo
wanga
wofoka
Aulimbikitsa.
Zokoma
ndi
zakuyanja
Zidzanditsatako;
Ndikhala
m'nyumba
ya
Mlungu
Ku
nthawi
zonsezo
Ku
madzi
ake
odikha
Anditsogolera;
Ndi
moyo
wanga
wofoka
Aulimbikitsa. (
Fade
out
with
steady
bass
and
percussion)