[male vocals] Oooooh,
aaaaah
Ambuye,
tisogolereni
Munthu
alibe
chabwino,
ngakhale
umuchitira
zabwino
Akapita
kupali,
alakula
zoipa
pa
moyo
wako
Ambuye
tizachita
bwanji,
pa
anthu
otelo
Chifukwa
ife
tilibe
kwina,
tigayende
kopanda
inu
noka
Yesu,
uli
pafupi,
tilindire
iwe
Yesu,
uli
pafupi,
tikhulupirire
iwe
Ambuyeee,
mutisogolere
Ambuyeee,
pa
moyo
wathu
Ambuyeee,
mutisogolere
Ambuyeee,
pa
moyo
wathu
You
are
our
Lord,
Alfa
and
Omega
The
beginning
and
the
end
Kulibe
wina
angathe,
kutithandiza
pa
moyo
wathu
Nthawi
zambiri
timasauka,
koma
iwe
uli
ndi
mphamvu
Ndiwe
woyera,
wamphamvu
zonse,
tikhulupirira
iwe
Glory,
yes
Lord,
amen
Ambuyeee,
mutisogolere
Ambuyeee,
pa
moyo
wathu
Ambuyeee,
mutisogolere
Ambuyeee,
pa
moyo
wathu
Tigopepa
inu
noka
Kuti
pamene
titandiza,
ena
akulakalaka
kufuna
tandizo
muti
chosele
zoipa
Koma
iwe
ndiwe
chishango
chathu
Iwe
ndiwe
mthunzi
wathu
Thank
you
Jesus,
praise
Him
Pa
njira
yopita
kumwamba,
mutitsogolere
Pa
mavuto
a
pa
dziko,
mutitsogolere
Palibe
monga
iwe,
wolunjika
mtima
wathu
Uli
ndi
chikondi,
uli
ndi
chifundo
Hallelujah,
yes
Lord
Ambuyeee,
mutisogolere
Ambuyeee,
pa
moyo
wathu
Ambuyeee,
mutisogolere
Ambuyeee,
pa
moyo
wathu
Ambuye,
tisogolereni
Pa
moyo
wathu
wonse
Ambuyeee,
pa
moyo
wathu
Ambuye,
tisogolereni
Pa
moyo
wathu
wonse
Ambuye,
tisogolereni
Amen,
amen,
amen
oooooooooho
aaaaaaaaaha
mcccjimmmmm