Frobits
🎵 A song made on Frobits

Holy Lord of All

0:000:00
Download
Reply with a song
Lyrics

[male

vocals] (

Soft

piano

chords

swelling

into

ambient

pads)

Inu

Mulungu,

tikuyamikani;

Tibvomereza

ndinu

Ambuyathu;

Ponse,

Atate,

akugwadirani,

Ndinu

wamuyaya!

Nanu

akukuzani

amithenga,

Nanu

zam’

mwamba

ndi

zamphamvu

zake,

Nanu

angelo

a

mitundu

yonse

Akuimbirani! “

Mbuye

Woyera!

E,

Woyera

nokha!

Mbuye

Woyera!

Mbuye

wa

makamu!

Ponse

ulemu

wanu

ndi

wodzaza

Pansi

ndi

Kumwamba.”

Nanu

Atumwi

akumveka

aja,

Ndi

Aneneri

oyanjana

omwe,

Ndi

aunyinji

anakuferani

Akuyamikani.

Mpingo

woyera

wa

kwa

anthu

onse

Ukumverani,

Mfumu

ndi

Atate,

Mwana

woona

wa

ulemu

wonse,

Mzimu

Nkhoswe

yemwe.

L

Kristu

Mfumuyo

yauleme

rero!

Mwana

wosatha

wa

Atate

ndinu!

Simunanyoza

mimba

ya

namwali

Potipulumutsa.

Imfa

mutagonjetsa

ndi

zowawa,

Njira

munatsegula

tikalowe

Momwe

mukhala

Inu

ndi

Atate

Mwaulemerero.

Kumva

milandu

yathu

mudzabwera

Mutithandize,

atumiki

anu;

Mwatiwombola

nawo

mwazi

wanu:

Mutipulumutse

Mtiwerengere

mMwamba

ndi

oyera;

Mutidalitse,

ndife

anthu

anu;

Moyo

wosatha

mutipatse

tonse,

Mutilamulire.

Tsiku

ndi

tsiku

timalemekeza;

Nanu

tikukuzani

osaleka;

Mbuye,

mtisunge

tingachimwe

lero:

Mtichitire

nsisi.

Mbuye,

chifundo

chanu

chitigwere

Monga

tikhulupira

Inu

nokha;

Ndakhulupira

zedi

mwanu,

Mbuye,

Ndisagome

konse!

Ndi

Aleluya

imbirani

'Tate

wathu,,

Analenga

zonse.

Chifundo

chake

chachikulu,

Nzeru,

mphamvu

ndi

ufumu

Tiyamike

tonse.

Ndi

Aleluya

imbirani

Yesu

Khristu

Mpulumutsi,

Anachoka

kwawo,

Nakhala

munthu,

pansi

pano,

Nasauka,

natifera,

Natisiyira

mawu.

Ndi

Aleluya

imbirani

Mzimu

wake

Wakuyera,

Amakhala

nafe.

Atilangiza

za

Mulungu,

Nayeretsanso

mitima

Ya

akhristu

ife.

Mulungu

wathu

tiyamika,

'Tate,

Mwana,

Mzimu

yemwe

Aleluya

Inu.

Woyera

Inu

ndi

wamphamvu,

Muyenera

anthu

onse

Agwadire

Inu.

Munthu

Wazisoniyo

Timtcha

dzina

lakelo,

Mpulumutsi

linanso;

Aleluya,

ndiye

Yesu.

Anapeputsidwako,

Nandifera

m'mtandamo,

Anandiwombolayo;

Aleluya,

ndiye

Yesu.

Ife

tinachimwadi,

Iye

sanachimwa

'yi,

Anachotsa

tchimoli,

Aleluya,

ndiye

Yesu.

Anapachikidwatu,

Natha

ntchito

yake

myu!

Anakwera

m'Mwamba

duu!

Aleluya,

ndiye

Yesu.

Adzabwera

Iyenso

Kudzatenga

akewo;

Nyimbo

tidzaimbanso,

Aleluya,

ndiye

Yesu.

Ooh,

we

lift

You

up

You

are

the

everlasting

King

We

bow

before

Your

throne (

Fading

piano

and

strings)

Amen.

More songs by Pastor Listen to songs created by others
FROBITS