Mverani
bwino…
bwino
Iyi
nkhani
ndikukufotokoza…
Ine
Prophetic
Professor
Fizwell…
Nkhani
ya
mayi
wolimba
mtima…
Zina
Lake
ni
Linet
Mwanza…
Ndi
nkhani
ya
mayi,
dzina
lake
Linet
Anali
ndi
banja,
moyo
unali
bwino
Koma
tsiku
lina,
imfa
inabwera
Mwamuna
wake
anamusiya
ndi
ana
atatu
Anyamata
okha
okha,
moyo
unavuta
Misozi
ndi
Mavuto,
tsiku
ndi
tsiku
Koma
sanasiye,
anaimirira
yekha
Kukhala
mayi
ndi
Tate
Panthawi
imodzi
Chikhulupiriro
cha
mayi,
sichisila
yayi
Mulungu
amaona,
amam’
teteza
Chikhulupiriro
cha
mayi,
sichisila
yayi
Mulungu
amaona,
amam’
teteza
Patapita
nthawi,
zaka
zitatu
Anakumana
ndi
bwenzi
lakale
Anapatsa
mtima
wake
mwayi
wachiwiri
Kukhulupirira
moyo
uzachinja
Anakwatirana,
na
ana
ena
anabwera
Banja
linakula,
chiyembekezo
chabwera
Koma
zaka
zili
four
pamene
zinafika
Mwamuna
anapondoka…
anasiya
banja
Anatsala
yekha
ndi
ana
ambiri
Zinakhala
zolemetsa
kuchila
kudala
Koma
mayi
ameneyo
sanagwe
pansi
Anapitiriza
kulimbikira
moyo
Chikhulupiriro
cha
mayi,
sichisila
yayi
Mulungu
amaona,
amam’
teteza
Chikhulupiriro
cha
mayi,
sichisila
yayi
Mulungu
amaona,
amam’
teteza
Umoyo
unaleta,
mayesero
ambiri
Anataya
mwana
wake,
Omega,
infa
Yatenga
Ululu
waukulu,
mtima
unalira
Koma
sanasiye
baana
Banasala
bake
Anatsala
ndi
ana
asanu
ndi
mmodzi
mtsikana
Ngakhale
Mabvuto
yanali
yakulu
Chikhulupiriro
chake
chinakhalabe
cholimba
Anapitiriza
kuyenda
ndi
Mulungu
Wake
Chikhulupiriro
cha
mayi,
sichisila
yayi
Mulungu
amaona,
amam’
teteza
Chikhulupiriro
cha
mayi,
sichisila
yayi
Mulungu
amaona,
amam’
teteza
Ankagwira
ntchito,
usiku
ndi
Kuseni
Nthawi
zina
ankakhala
opanda
pokhala
Koma
sanasiye,
anakhulupirira
Mulungu
Pang’
ono
ndi
pang’
ono
zinthu
zinasintha
Anamanga
nyumba,
ndi
manja
ake
Kuchokera
pa
kusowa
kufika
pa
kukhala
Banja
silinathandize,
anali
yekha
Koma
Mulungu
anali
naye
nthawi
zonse
Lero
madalitso
akuonekera
Kupyolera
mubana
bake
Mayi
ameneyo
ndi
survivor
Ndipo
ndi
winner
weni-weni
Chikhulupiriro
cha
mayi,
sichisila
yayi
Mulungu
amaona,
amam’
teteza
Chikhulupiriro
cha
mayi,
sichisila
yayi
Mulungu
amaona,
amam’
teteza
Iyi
ndi
nkhani
ya
Linet
Mwanza…
Mayi
wolimba
Chikhulupiriro …
Ine
Prophetic
Professor
Fizwell…
ndikukuuza…
Ngakhale
moyo
uli
wovuta…
Musasiye…
Chifukwa
Mulungu
amaona…