[male vocals] Piano
chords
playing 1
Ndi
Aleluya
imbirani
'Tate
wathu,
wakumwamba,
Analenga
zonse.
Chifundo
chake
chachikulu,
Nzeru,
mphamvu
ndi
ufumu
Tiyamike
tonse. 2
Ndi
Aleluya
imbirani
Yesu
Khristu
Mpulumutsi,
Anachoka
kwawo,
Nakhala
munthu,
pansi
pano,
Nasauka,
natifera,
Natisiyira
mawu. 3
Ndi
Aleluya
imbirani
Mzimu
wake
Wakuyera,
Amakhala
nafe.
Atilangiza
za
Mulungu,
Nayeretsanso
mitima
Ya
akhristu
ife. 4
Mulungu
wathu
tiyamika,
'Tate,
Mwana,
Mzimu
yemwe
Aleluya
Inu.
Woyera
Inu
ndi
wamphamvu,
Muyenera
anthu
onse
Agwadire
Inu.