[male vocals] Aleluyaaaa,
aleluyaaaa
Ooh,
Mlengi
wathu,
tiyeni
tilambire
Mulongozi
wane,
musogoreli
wanga
Muvikilili
wane,
muchingilizi
wanga
Nthawi
zonse
ndikhala
nanu
pafupi
Nkhondo
zanga
zonse
imwe
mukuzidziwa
Nimenyereni
adani,
ndilibe
mphamvu
Nthawi
zonse
ndili
pansi
pa
mapiko
anu
Nkhondo
zanga
zonse
imwe
mukuzidziwa
Nimenyereni
adani,
ndilibe
mphamvu
Aleluya
amen,
aleluya
amen
Aleluya
amen,
aleluya
aleluyaaaa
Mulungu
wamoyo,
wosalephera
Aleluya
amen,
aleluya
amen
Aleluya
amen,
aleluya
amen
Nazizipizya
vyalema,
zonse
zimandidetsa
nkhawa
Nivwirani
Tata,
musandisiye
ndekha
Imwe
mukumanya
mazuba
ya
umoyo
wane
Kalonga
wamutende,
mtendere
weniweni
Satana
akundinamiza,
akufuna
kundilekanitsa
Koma
ndimukhulupirira
Yesu,
mwini
wa
mphamvu
Zonse
zimene
Satana
waika
pa
moyo
wane
Chotsani
zonse,
muzichotse
mwamsanga
Aleluya
amen,
aleluya
amen
Aleluya
amen,
aleluya
aleluyaaaa
Aleluya
amen,
aleluya
amen
Aleluya
amen,
aleluya
aleluyaaaa
Mulungu
wamoyo,
wosalephera
Aleluya
amen,
aleluya
amen
Imwe
ndinu
mpulumutsi
wane,
ndikudziwa
Sadzandiiwala,
sindingafunike
mantha
Ndikuyenda
nanu,
Yesu
Kristu
Khalani
nane,
lankhulani
nane
Zonse
zili
mmanja
mwanu,
ndikupembedza
Yesu
Kristu,
khalani
nane
Aleluya
amen,
aleluya
amen
Aleluya
amen,
aleluya
aleluyaaaa
Aleluya
amen,
aleluya
amen
Aleluya
amen,
aleluya
aleluyaaaa
Mulungu
wamoyo,
wosalephera
Aleluya
amen,
aleluya
amen
Aleluya
amen,
aleluya
amen
Zikomo
Ambuye
Yesu
Kristu
Khalani
nane,
lankhulani
nane
Yesu
Kristu,
amen
Aleluyaaaa,
amen