[male vocals] Ndikonda
Mlungu
pomva
Mbuye
wanga
Amva
pemphero
ndi
kulira
kwanga,
Namatchereza
khutu
nditapfuula,
Andithandiza,
nandipulumutsa.
Andithandiza,
nandipulumutsa.
Andithandiza,
nandipulumutsa.
Mulungu
wanga
ndiye
wachifundo
Ndiwolungama
mtima
ndi
wabwino;
Apulumutsa
anthu
akufoka,
Akathandiza
nkhawa
imachoka.
Akathandiza
nkhawa
imachoka.
Akathandiza
nkhawa
imachoka.
Akathandiza
nkhawa
imachoka.
Mtimanga,
bwera
kuti
upumule,
Wakuchitiranso
zokoma
Mbuye,
Wakuchotsera
imfa
ndi
misozi,
Ndingakhumudwe
asungira
phazi.
Ndingakhumudwe
asungira
phazi.
Ndingakhumudwe
asungira
phazi.
Nditani
ine
kubwezera
Mbuye
Zokoma
zonse
anandichitira?
Chipulumutso
chake
ndidzatama,
Ndinalumbira
zija
ndidzapatsa.
Imfa
ya
anthu
ake
imkomera,
Awalandira
m'nyumba
zokonzeka,
Mbuye,
kapolo
wanu
ndipereka
Nsembeyi
yonga
yanu,
ndine
ndekha.
Nsembeyi
yonga
yanu,
ndine
ndekha.
Nsembeyi
yonga
yanu,
ndine
ndekha.
Mtima
wanga
uyamike
Mfumu
Yakumwambako;
Anandiwombola
ine
Nanditsuka
m'mtimamo.
Ife
tonse,
ife
tonse,
Tiyamike
Mlunguyo.
Ife
tonse,
ife
tonse,
Tiyamike
Mlunguyo.
Ife
tonse,
ife
tonse,
Tiyamike
Mlunguyo.
Tiyamike
Mlungu
wathu
Kaamba
ka
chifundocho;
Nthawi
zonse
sasanduka
Mlungu
wathu
yemweyo.
Nthawi
zonse
sasanduka
Mlungu
wathu
yemweyo.
Nthawi
zonse
sasanduka
Mlungu
wathu
yemweyo.
Nthawi
zonse
monga
'Tate
Atisamaliratu,
Atisunga
m'manja
mwake,
Atipulumutsatu.
Nthawi
zonse
sasanduka
Mlungu
wathu
yemweyo.
Anthu
a
mitundu
yonse,
Ndipo
a
Kumwambako,
Yamikani
Mlungu
wathu,
Ndiye
wakukomatu.
Anthu
onse,
anthu
onse,
Yamikani
Mlunguyo.
Anthu
onse,
anthu
onse,
Yamikani
Mlunguyo.
Msandipitire,
Yesu,
Mundimvere
ine;
Mulikudalitsa
ena,
Msandipitirire
Yesu
Mbuye,
Khutu
munditchere
M'mene
muitana
ena
Msandipitirire.
Ndigwadira
Inu,
Yesu,
Musandikanize;
Ndikalapatu
machimo
Mbuye,
mndithandize.
Nkhope
yanu
ndifunitsa,
Sind'yenera
konse;
M'mtima
mwanga
muchiritse
Nthenda
zanga
zonse.