Frobits
🎵 A song made on Frobits

Lord Be With Me (Remix)

0:000:00
Download
Reply with a song
Lyrics

[male

vocals] (

Reggae

rhythm

kicks

in

with

a

steady

bassline)

Yesu,

yesu,

yesu.

Mundimvere,

Mbuye

wanga

Nkana

ine

ndimalakwa,

Koma

ndinu

moyo

wanga;

Mbuye,

mkhale

ndine.

Mbuye,

mkhale

ndine.

Mbuye,

mkhale

ndine

Mbuye,

mkhale

ndine

Ndine

mlendo

pansi

pano,

Msanditaye

m'dzanja

lanu,

Mundisunge

mwana

wanu;

Mbuye,

mkhale

ndine.

Mbuye,

mkhale

ndine.

Mbuye,

mkhale

ndine

Mbuye,

mkhale

ndine

Munafera

ine

kale

Kuti

mukandimasule,

Lero

lino

mndinyamule;

Mbuye,

mkhale

ndine.

Mbuye,

mkhale

ndine.

Mbuye,

mkhale

ndine

Mbuye,

mkhale

ndine

Mundidzze

ndi

chikondi,

Mndiyeretse

m'mtima

monse,

Chifuniro

change

mthyole;

Mbuye,

mkhale

ndine.

Mbuye,

mkhale

ndine.

Mbuye,

mkhale

ndine

Mbuye,

mkhale

ndine

Imfa

ikandifikira,

Inu

ndidzakangamira;

Ndikalowa

ine

m'mdima,

Mbuye,

mkhale

ndine.

Mbuye,

mkhale

ndine.

Mbuye,

mkhale

ndine

Mbuye,

mkhale

ndine

Yehova,

Mbusa

wangadi,

Ndilibe

kusowa;

Andigonetsa

bwinoli

Mumsipu

wokoma.

Cha

dzina

lakelo.

Ku

madzi

ake

odikha

Anditsogolera;

Ndi

moyo

wanga

wofoka

Aulimbikitsa.

Anditsogolera

m'njira

Zakulungamazo;

Chifukwa

changaay',

koma

Ku

madzi

ake

odikha

Anditsogolera;

Ndi

moyo

wanga

wofoka

Aulimbikitsa.

Ndipyola

kodi

chikhwawa

Cha

mthunzi

wa

imfa?

Ndilibe

mantha

ngati

'Nu

Mundiperekeza.

Ku

madzi

ake

odikha

Anditsogolera;

Ndi

moyo

wanga

wofoka

Aulimbikitsa.

Chakudya

changa

chabwino

Mwandikonzera

pha!

Pamaso

pa

adaniwo

Mudyetse

mtimanga.

Ku

madzi

ake

odikha

Anditsogolera;

Ndi

moyo

wanga

wofoka

Aulimbikitsa.

Mwadzoza

mutu

wanga

ndi

Mafuta

okoma,

Mwadzaza

chikho

changadi,

Inde,

chisefuka.

Ku

madzi

ake

odikha

Anditsogolera;

Ndi

moyo

wanga

wofoka

Aulimbikitsa.

Zokoma

ndi

zakuyanja

Zidzanditsatako;

Ndikhala

m'nyumba

ya

Mlungu

Ku

nthawi

zonsezo

Ku

madzi

ake

odikha

Anditsogolera;

Ndi

moyo

wanga

wofoka

Aulimbikitsa.

Inu

Mulungu,

tikuyamikani;

Tibvomereza

ndinu

Ambuyathu;

Ponse,

Atate,

akugwadirani,

Ndinu

wamuyaya!

Nanu

akukuzani

amithenga,

Nanu

zam’

mwamba

ndi

zamphamvu

zake,

Nanu

angelo

a

mitundu

yonse

Akuimbirani! “

Mbuye

Woyera!

E,

Woyera

nokha!

Mbuye

Woyera!

Mbuye

wa

makamu!

Ponse

ulemu

wanu

ndi

wodzaza

Pansi

ndi

Kumwamba.”

Nanu

Atumwi

akumveka

aja,

Ndi

Aneneri

oyanjana

omwe,

Ndi

aunyinji

anakuferani

Akuyamikani.

Mpingo

woyera

wa

kwa

anthu

onse

Ukumverani,

Mfumu

ndi

Atate,

Mwana

woona

wa

ulemu

wonse,

Mzimu

Nkhoswe

yemwe.

Kristu

Mfumuyo

yauleme

rero!

Mwana

wosatha

wa

Atate

ndinu!

Simunanyoza

mimba

ya

namwali

Potipulumutsa.

Imfa

mutagonjetsa

ndi

zowawa,

Njira

munatsegula

tikalowe

Momwe

mukhala

Inu

ndi

Atate

Mwaulemerero.

Kumva

milandu

yathu

mudzabwera

Mutithandize,

atumiki

anu;

Mwatiwombola

nawo

mwazi

wanu:

Mutipulumutse

Mtiwerengere

mMwamba

ndi

oyera;

Mutidalitse,

ndife

anthu

anu;

Moyo

wosatha

mutipatse

tonse,

Mutilamulire.

Tsiku

ndi

tsiku

timalemekeza;

Nanu

tikukuzani

osaleka;

Mbuye,

mtisunge

tingachimwe

lero:

Mtichitire

nsisi.

Mbuye,

chifundo

chanu

chitigwere

Monga

tikhulupira

Inu

nokha;

Ndakhulupira

zedi

mwanu,

Mbuye,

Ndisagome

konse!

Mbuye,

chifundo

chanu

chitigwere

Monga

tikhulupira

Inu

nokha;

Mbuye,

mkhale

ndine

Ndine

mlendo

pansi

pano,

Msanditaye

m'dzanja

lanu,

Mundisunge

mwana

wanu;

Mbuye,

mkhale

ndine.

Mbuye,

mkhale

ndine.

Mbuye,

mkhale

ndine

Mbuye,

mkhale

ndine

Ndine

mlendo

pansi

pano,

Msanditaye

m'dzanja

lanu,

Mundisunge

mwana

wanu;

Mbuye,

mkhale

ndine.

More songs by israel Listen to songs created by others
FROBITS