Ana
inu…
mverani
bwino…
Kubadwira
m’
banja
lolemera,
sikutanthauza
kuti
mudzakhala
olemera.
Kubadwira
m’
banja
losauka,
sikutanthauza
kuti
mudzakhala
osauka.
Tsogolo
lanu
lili
m’
manja
mwanu…
Aliyense
ali
ndi
umoyo
wake…
Tiyeni… --- ##
[Verse 1] Ninaona
mnyamata,
anabadwira
m’
banja
lolemera,
nyumba
yabwino,
galimoto,
sukulu
yabwino.
Koma
anatsatira
anzake
oyipa,
mowa
ndi
mankhwala
osokoneza
bongo,
anasiya
sukulu.
Lero
ali
m’
misewu,
akupempha
ndalama,
chuma
cha
makolo
chatha,
dzina
lawonongeka.
Ninaonanso
mtsikana,
anabadwira
m’
nyumba
ya
matabwa,
amayi
ake
ankagulitsa
tomato.
Usiku
ankaphunzira
ndi
kandulo,
osataya
mtima.
Lero
ndi
namwino,
wamangira
makolo
ake
nyumba.
M’
banja
losauka…
mungatuluke
olemera. --- ##
[Pre-Chorus] Mverani
ana
inu…
Kulemera
kapena
kusauka
sizimasankha
tsogolo
lanu.
Tsogolo
lanu
lili
mwa
inu.
Gwirani
ntchito…
pempherani…
musataye
mtima. --- ## [
Chorus] **
Gwirani
ntchito
mwana
we!** **
Mulungu
akutsogolereni.** **
Mulungu
akutetezeni** **
ku
zinthu
zonse
zoononga
moyo.** **
Osasiya
sukulu,
ndiyo
kiyi
ya
tsogolo
lanu!** **
Osasiya
sukulu,
ndiyo
njira
ya
kupambana!** **
Tsogolo
la
m’
badwo
wanu
lili
mwa
inu.** **
M’
banja
losauka
mungatuluke
olemera.** **
M’
banja
lolemera
mungakhale
osauka.** **
Aliyense
ali
ndi
umoyo
wake…** **
Future
yanu
ili
m’
manja
mwanu.**
Musatsatire
anzanu
mwakhungu.
Akati, “
Tiyeni
tikamwe,”
kapena “
Tiyeni
tikabe,”
inu
nenani, “
Ayi!”
Mukudziwa
komwe
mukupita.
Maphunziro,
pemphero
ndi
ntchito
ndizo
zida
zanu.
Foni
yabwino
siimakupangani
munthu,
zovala
zamtengo
sizimakupangani
munthu.
Munthu
amadziwika
ndi
khalidwe
lake,
ndi
ntchito
yake,
ndi
Mulungu
wake.
Mwana
wanga…
dziko
lili
ndi
mayesero
ambiri.
Anzake
oyipa,
mowa,
mankhwala
osokoneza
bongo…
zonsezi
zimafuna
kuwononga
moyo
wako.
Koma
ngati
Mulungu
ali
nawe,
palibe
chingakugwetse.
Banja
lako
likuyang’
ana
iwe.
Dzina
la
banja
lako
lili
m’
manja
mwako.
Usalole
kuti
lithere
pa
iwe. **
Gwirani
ntchito
mwana
we!** **
Mulungu
akutsogolereni!** **
Mulungu
akutetezeni!** **
Pewani
anzake
oyipa,
pewani
zoipa
zonse.** **
Osasiya
sukulu,
ndiyo
kiyi
ya
tsogolo
lanu!** **
Osasiya
sukulu,
ndiyo
njira
ya
kupambana!** **
M’
banja
losauka
mungatuluke
olemera.** **
M’
banja
lolemera
mungakhale
osauka.** **
Aliyense
ali
ndi
umoyo
wake…** **
Future
yanu
ili
m’
manja
mwanu.** **
Gwirani
ntchito…
pempherani…
phunzirani…** **
musataye
mtima!** **
Gwirani
ntchito…
pempherani…
phunzirani…** **
musataye
mtima!**
Kubadwira
m’
banja
lolemera…
sikutanthauza
kuti
mudzakhala
olemera.
Kubadwira
m’
banja
losauka…
sikutanthauza
kuti
mudzakhala
osauka.
Tsogolo
lanu
lili
m’
manja
mwanu.
Pempherani…
phunzirani…
gwirani
ntchito…
Mulungu
akudalitseni
ana
anga.
Aliyense…
ali
ndi…
umoyo
wake…
Kachigamba
family
boys
susack
music
production